Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 15:29 - Buku Lopatulika

29 Ngati si kutero, adzachita chiyani iwo amene abatizidwa chifukwa cha akufa? Ngati akufa saukitsidwa konse, abatizidwa chifukwa ninji chifukwa cha iwo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ngati si kutero, adzachita chiyani iwo amene abatizidwa chifukwa cha akufa? Ngati akufa saukitsidwa konse, abatizidwa chifukwa ninji chifukwa cha iwo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Ngati Yesu sadauke kwa akufa, nanga amafunanji anthu amene amabatizidwa m'malo mwa amene adafa? Ngati akufa sauka konse, nanga chifukwa chiyani anthu amabatizidwa m'malo mwao?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Tsono ngati kulibe kuuka kwa akufa, kodi iwo amene akubatizidwa chifukwa cha akufa, adzatani? Ngati akufa saukitsidwa nʼkomwe, bwanji nanga anthu akubatizidwa mʼmalo mwawo?

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 15:29
7 Mawu Ofanana  

Koma Yesu anayankha nati, Inu simudziwa chimene mupempha. Kodi mukhoza kumwera chikho nditi ndidzamwere Ine? Iwo ananena kwa Iye, Ife tikhoza.


nabatizidwa ndi iye mu mtsinjewo wa Yordani, alikuwulula machimo ao.


Pakuti ngati akufa saukitsidwa, Khristunso sanaukitsidwe;


Ndipo pamene zonsezo zagonjetsedwa kwa Iye, pomwepo Mwana yemwe adzagonjetsedwa kwa Iye amene anamgonjetsera zinthu zonse, kuti Mulungu akhale zonse mu zonse.


Nanga ifenso tili m'moopsa bwanji nthawi zonse?


Ngati ndinalimbana ndi zilombo ku Efeso monga mwa munthu, ndipindulanji? Ngati akufa saukitsidwa, tidye timwe pakuti mawa timwalira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa