1 Akorinto 15:23 - Buku Lopatulika23 Koma yense m'dongosolo lake la iye yekha, chipatso choyamba Khristu; pomwepo iwo a Khristu, pakubwera kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma yense m'dongosolo lake la iye yekha, chipatso choundukula Khristu; pomwepo iwo a Khristu, pakubwera kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Koma aliyense adzauka pa nthaŵi yake: woyambirira ndi Khristu, ndipo pambuyo pake, pamene Khristuyo adzabwera, nawonso amene ali ake adzauka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Koma aliyense adzauka pa nthawi yake. Khristu ndiye woyambirira, pambuyo pake, pamene Khristu adzabwera, iwo amene ali ake adzauka. Onani mutuwo |