1 Akorinto 15:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti monga mwa Adamu onse amwalira, choteronso mwa Khristu onse akhalitsidwa ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti monga mwa Adamu onse amwalira, choteronso mwa Khristu onse akhalitsidwa ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Monga anthu onse amamwalira chifukwa ndi ana a Adamu, momwemonso anthu onse adzauka chifukwa cholumikizana ndi Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pakuti monga mwa Adamu onse amafa, chomwechonso mwa Khristu onse adzakhala ndi amoyo. Onani mutuwo |