1 Akorinto 15:19 - Buku Lopatulika19 Ngati tiyembekezera Khristu m'moyo uno wokha, tili ife aumphawi oposa a anthu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ngati tiyembekezera Khristu m'moyo uno wokha, tili ife aumphawi oposa a anthu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ngati taika chikhulupiriro chathu mwa Khristu chifukwa cha moyo uno wokha, ndiye kuti ndife omvetsa chisoni koposa anthu ena onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ngati kukanakhala kuti tili ndi chiyembekezo mwa Khristu mʼmoyo uno wokha, tikanakhala omvetsa chisoni kuposa anthu ena onse. Onani mutuwo |