1 Akorinto 15:18 - Buku Lopatulika18 Chifukwa chake iwonso akugona mwa Khristu anatayika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Chifukwa chake iwonso akugona mwa Khristu anatayika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pamenepo nawonso amene adamwalira ali okhulupirira Khristu, adatayika ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndiye kuti nawonso amene agona tulo mwa Ambuye ndi otayika. Onani mutuwo |