Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 15:18 - Buku Lopatulika

18 Chifukwa chake iwonso akugona mwa Khristu anatayika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Chifukwa chake iwonso akugona mwa Khristu anatayika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pamenepo nawonso amene adamwalira ali okhulupirira Khristu, adatayika ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndiye kuti nawonso amene agona tulo mwa Ambuye ndi otayika.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 15:18
6 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene anagwada pansi, anafuula ndi mau aakulu, Ambuye, musawaikire iwo tchimo ili. Ndipo m'mene adanena ichi, anagona tulo.


pomwepo anaoneka pa nthawi imodzi kwa abale oposa mazana asanu, amene ochuluka a iwo akhala kufikira tsopano, koma ena agona;


Pakuti ichi tinena kwa inu m'mau a Ambuye, kuti ife okhala ndi moyo, otsalira kufikira kufikanso kwa Ambuye, sitidzatsogolera ogonawo.


Pakuti Ambuye adzatsika Kumwamba mwini yekha ndi mfuu, ndi mau a mngelo wamkulu, ndi lipenga la Mulungu; ndipo akufa mwa Khristu adzayamba kuuka;


Ndipo ndinamva mau ochokera Kumwamba, ndi kunena, Lemba, Odala akufa akumwalira mwa Ambuye, kuyambira tsopano; inde, anena Mzimu, kuti akapumule ku zolemetsa zao; pakuti ntchito zao zitsatana nao pamodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa