Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 14:40 - Buku Lopatulika

40 Koma zonse zichitike koyenera ndi kolongosoka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Koma zonse zichitike koyenera ndi kolongosoka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Koma tsono, zonse zizichitika moyenera ndi molongosoka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Koma chilichonse chichitike moyenera ndi mwadongosolo.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 14:40
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Akalonga onse, yense pa tsiku lake, apereke zopereka zao za kupereka chiperekere guwa la nsembe.


Tiyendeyende koyenera, monga usana; si m'madyerero ndi kuledzera ai, si m'chigololo ndi chonyansa ai, si mu ndeu ndi nkhwidzi ai.


Ngati wina ali ndi njala adye kwao; kuti mungasonkhanire kwa chiweruziro. Koma zotsalazo ndidzafotokoza pakudza ine.


Pakuti ndingakhale ndili kwina m'thupi, komatu mumzimu ndili pamodzi ndi inu, wokondwera pakupenya makonzedwe anu, ndi chilimbiko cha chikhulupiriro chanu cha kwa Khristu.


Chifukwa cha ichi ndinakusiya iwe mu Krete, kuti ukalongosole zosowa, nukaike akulu m'midzi yonse, monga ndinakulamulira;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa