1 Akorinto 14:34 - Buku Lopatulika34 Akazi akhale chete mu Mipingo. Pakuti sikuloledwa kwa iwo kulankhula. Koma akhale omvera, monganso chilamulo chinena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Akazi akhale chete m'Mipingo. Pakuti sikuloledwa kwa iwo kulankhula. Koma akhale omvera, monganso chilamulo chinena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 akazi akhale chete m'misonkhano ya mpingo, pakuti iwo saloledwa kulankhula. Monga Malamulo a Mose anenera, akazi azikhala omvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Amayi akhale chete mʼmisonkhano ya mpingo. Iwo asaloledwe kuyankhula, koma azikhala omvera monga mmene lamulo linenera. Onani mutuwo |