1 Akorinto 14:32 - Buku Lopatulika32 ndipo mizimu ya aneneri imvera aneneri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 ndipo mizimu ya aneneri imvera aneneri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Anthu amene ali ndi mphatso ya kulankhula mau ochokera kwa Mulungu, adziŵe kuilamulira mphatsoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Mizimu ya aneneri imamvera ulamuliro wa aneneri. Onani mutuwo |