1 Akorinto 14:30 - Buku Lopatulika30 Koma ngati kanthu kuvumbulutsidwa kwa wina wakukhalapo, akhale chete woyambayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma ngati kanthu kuvumbulutsidwa kwa wina wakukhalapo, akhale chete woyambayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Koma Mulungu akaulula kanthu kwa munthu wina amene ali pomwepo, amene akulankhulayo akhale chete. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ndipo ngati vumbulutso labwera kwa munthu amene wakhala pansi, amene akuyankhulayo akhale chete. Onani mutuwo |