1 Akorinto 14:20 - Buku Lopatulika20 Abale, musakhale ana m'chidziwitso, koma m'choipa khalani makanda, koma m'chidziwitso akulu misinkhu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Abale, musakhale ana m'chidziwitso, koma m'choipa khalani makanda, koma m'chidziwitso akulu misinkhu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Abale, musamaganiza zachibwana. Pa zoipa, khalani ngati ana osadziŵa, koma pa maganizo anu, mukhale okhwima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Abale, lekani kuganiza ngati ana. Mukhale ana pa nkhani ya zoyipa koma mʼmaganizo anu mukhale okhwima. Onani mutuwo |