Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 14:18 - Buku Lopatulika

18 Ndiyamika Mulungu kuti ndilankhula malilime koposa inu nonse;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndiyamika Mulungu kuti ndilankhula malilime koposa inu nonse;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ndikuthokoza Mulungu kuti ine ndimalankhula m'zilankhulo zosadziŵika kuposa nonsenu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndikuyamika Mulungu chifukwa ndimayankhula malilime kuposa nonsenu.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 14:18
7 Mawu Ofanana  

Pakutitu iwe uyamika bwino, koma winayo samangiriridwe.


koma mu Mpingo ndifuna kulankhula mau asanu ndi zidziwitso changa, kutinso ndikalangize ena, koposa kulankhula mau zikwi m'lilime.


Pakuti iye wakulankhula lilime salankhula ndi anthu, koma ndi Mulungu; pakuti palibe munthu akumva; koma mumzimu alankhula zinsinsi.


Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.


Ndipo ndifuna inu nonse mulankhule malilime, koma makamaka kuti mukanenere; ndipo wakunenera aposa wakulankhula malilime, akapanda kumasulira, kuti Mpingo ukalandire chomangirira.


Pakuti akusiyanitsa iwe ndani? Ndipo uli nacho chiyani chosati wachilandira? Koma ngati wachilandira udzitamanda bwanji, monga ngati sunachilandire?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa