Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 14:17 - Buku Lopatulika

17 Pakutitu iwe uyamika bwino, koma winayo samangiriridwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Pakutitu iwe uyamika bwino, koma winayo samangiriridwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Ngakhale inu muthokoze Mulungu bwinobwino, koma munthu winayo sapindulapo konse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mukhoza kumathokoza mokwanira, koma munthu winayo sanathandizikepo.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 14:17
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake tilondole zinthu za mtendere, ndi zinthu zakulimbikitsana wina ndi mnzake.


Ndiyamika Mulungu kuti ndilankhula malilime koposa inu nonse;


Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.


Ndipo ndifuna inu nonse mulankhule malilime, koma makamaka kuti mukanenere; ndipo wakunenera aposa wakulankhula malilime, akapanda kumasulira, kuti Mpingo ukalandire chomangirira.


Koma tsopano, abale, ngati ndidza kwa inu ndi kulankhula malilime, ndikakupindulitsani chiyani, ngati sindilankhula ndi inu kapena m'vumbulutso, kapena m'chidziwitso, kapena m'chinenero, kapena m'chiphunzitso?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa