Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 14:14 - Buku Lopatulika

14 Pakuti ngati ndipemphera m'lilime, mzimu wanga upemphera, koma chidziwitso changa chikhala chosabala kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Pakuti ngati ndipemphera m'lilime, mzimu wanga upemphera, koma chidziwitso changa chikhala chosabala kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Ngati ndipemphera m'chilankhulo chosadziŵika, mtima wanga ukupemphera inde, koma nzeru zanga sizipindulapo kanthu pamenepo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Popeza ngati ndipemphera mʼmalilime, ndi mzimu wanga umene ukupemphera, koma nzeru zanga sizikupindula kanthu.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 14:14
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake wolankhula lilime, apemphere kuti amasule.


koma mu Mpingo ndifuna kulankhula mau asanu ndi zidziwitso changa, kutinso ndikalangize ena, koposa kulankhula mau zikwi m'lilime.


Pakuti iye wakulankhula lilime salankhula ndi anthu, koma ndi Mulungu; pakuti palibe munthu akumva; koma mumzimu alankhula zinsinsi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa