1 Akorinto 14:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake wolankhula lilime, apemphere kuti amasule. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake wolankhula lilime, apemphere kuti amasule. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nchifukwa chake munthu wolankhula chilankhulo chosadziŵika, apemphere kuti alandirenso mphatso ya kuchitanthauzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pa chifukwa ichi munthu amene amayankhula malilime apemphere kuti azitha kutanthauzira zimene akunena. Onani mutuwo |