1 Akorinto 12:31 - Buku Lopatulika31 Koma funitsitsani mphatso zoposa. Ndipo ndikuonetsani njira yokoma yoposatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma funitsitsani mphatso zoposa. Ndipo ndikuonetsani njira yokoma yoposatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Iyai, koma inu muike mtima wanu pa mphatso zopambana. Tsonotu ndikuwonetseni njira yopambana kwenikweni: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Koma funitsitsani mphatso zopambana. Tsopano ndikuonetsani njira yopambana kwambiri. Onani mutuwo |