Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 12:31 - Buku Lopatulika

31 Koma funitsitsani mphatso zoposa. Ndipo ndikuonetsani njira yokoma yoposatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Koma funitsitsani mphatso zoposa. Ndipo ndikuonetsani njira yokoma yoposatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Iyai, koma inu muike mtima wanu pa mphatso zopambana. Tsonotu ndikuwonetseni njira yopambana kwenikweni:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Koma funitsitsani mphatso zopambana. Tsopano ndikuonetsani njira yopambana kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 12:31
8 Mawu Ofanana  

Odala ali akumva njala ndi ludzu la chilungamo; chifukwa adzakhuta.


koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye.


Ndingakhale ndilankhula malilime a anthu, ndi a angelo, koma ndilibe chikondi, ndikhala mkuwa woomba, kapena nguli yolira.


Tsatani chikondi; koma funitsitsani mphatso zauzimu, koma koposa kuti mukanenere.


Chifukwa chake, abale anga, funitsitsani kunenera, ndipo musaletse kulankhula malilime.


Koma za zoperekedwa nsembe kwa mafano: Tidziwa kuti tili nacho chidziwitso tonse. Chidziwitso chitukumula, koma chikondi chimangirira.


Komatu zenizeninso ndiyesa zonse zikhale chitayiko chifukwa cha mapambanidwe a chizindikiritso cha Khristu Yesu Ambuye wanga, chifukwa cha Iyeyu ndinatayikitsa zinthu zonse, ndipo ndiziyesa zapadzala, kuti ndikadzionjezere Khristu,


Ndi chikhulupiriro Abele anapereka kwa Mulungu nsembe yoposa ija ya Kaini, imene anachitidwa umboni nayo kuti anali wolungama; nachitapo umboni Mulungu pa mitulo yake; ndipo momwemo iye, angakhale adafa alankhulabe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa