1 Akorinto 12:25 - Buku Lopatulika25 kuti kusakhale chisiyano m'thupi; koma kuti ziwalo zifanane ndi kusamalana china ndi chinzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 kuti kusakhale chisiyano m'thupi; koma kuti ziwalo zifanane ndi kusamalana china ndi chinzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Adachita zimenezi kuti pasakhale kugaŵikana m'thupi, koma kuti ziwalo zonse zizisamalirana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 kuti pasakhale kugawikana mʼthupi koma kuti ziwalo zonse zisamalirane. Onani mutuwo |