Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 12:24 - Buku Lopatulika

24 Koma zokoma zathu zilibe kusowa; koma Mulungu analumikizitsa thupi, napatsa ulemu wochuluka kwa chosowacho;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Koma zokoma zathu zilibe kusowa; koma Mulungu analumikizitsa thupi, napatsa ulemu wochuluka kwa chosowacho;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Koma zimene zili zooneka bwino, nkosafunikira kuti tiziveke motero. Mulungu polumikiza ziwalo za thupi, adazilumikiza mwa njira yoti adapereka ulemu woposa kwa ziwalo zimene zimausoŵadi ulemuwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Koma ziwalo zooneka bwino, nʼkosafunika kuti tizisamalire mwapadera. Mulungu polumikiza ziwalo zathupi, anapereka ulemu wopambana kwa ziwalo zimene zimafunadi ulemuwo

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 12:24
5 Mawu Ofanana  

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.


Ndipo anati, Ndani anakuuza iwe kuti uli wamaliseche? Kodi wadya za mtengo uja, umene ndinakuuza iwe kuti usadye?


Koma ngati diso lako lamanja likulakwitsa iwe, ulikolowole, nulitaye; pakuti nkwabwino kwa iwe, kuti chimodzi cha ziwalo zako chionongeke, losaponyedwa thupi lako lonse mu Gehena.


ndipo zimene tiziyesa zochepa ulemu m'thupi, pa izi tiika ulemu wochuluka woposa; ndi zinthu zosakoma zikhala nacho chokometsera choposa.


kuti kusakhale chisiyano m'thupi; koma kuti ziwalo zifanane ndi kusamalana china ndi chinzake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa