Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 12:20 - Buku Lopatulika

20 Koma tsopano pali ziwalo zambiri, koma thupi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma tsopano pali ziwalo zambiri, koma thupi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Komatu ziwalo nzambiri, ngakhale thupi ndi limodzi lokha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Mmene zililimu, pali ziwalo zambiri koma thupi ndi limodzi lokha.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 12:20
5 Mawu Ofanana  

chomwecho ife, ndife ambiri, tili thupi limodzi mwa Khristu, ndi ziwalo zinzake, wina ndi wina.


Pakuti monga thupi lili limodzi, nilikhala nazo ziwalo zambiri; koma ziwalo zonse za thupilo, pokhala zambiri, zili thupi limodzi; momwemonso Khristu.


Pakutinso thupi silikhala chiwalo chimodzi, koma zambiri.


Koma ngati zonse zikadakhala chiwalo chimodzi, likadakhala kuti thupi?


Ndipo diso silingathe kunena kwa dzanja, Sindikufuna iwe, kapenanso mutu kwa mapazi, Sindikufunani inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa