Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 12:19 - Buku Lopatulika

19 Koma ngati zonse zikadakhala chiwalo chimodzi, likadakhala kuti thupi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Koma ngati zonse zikadakhala chiwalo chimodzi, likadakhala kuti thupi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ziwalo zonse zikadangokhala chiwalo chimodzi, sipakadakhala thupi konse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Nanga zonse zikanakhala chiwalo chimodzi, ndiye thupi likanakhala lotani?

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 12:19
3 Mawu Ofanana  

Pakutinso thupi silikhala chiwalo chimodzi, koma zambiri.


Koma tsopano, Mulungu anaika ziwalo zonsezo m'thupi, monga anafuna.


Koma tsopano pali ziwalo zambiri, koma thupi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa