Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 12:14 - Buku Lopatulika

14 Pakutinso thupi silikhala chiwalo chimodzi, koma zambiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Pakutinso thupi silikhala chiwalo chimodzi, koma zambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Thupitu si chiwalo chimodzi chokha ai, koma lili ndi ziwalo zambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Tsopano thupi silinapangidwe ndi chiwalo chimodzi koma ndi ziwalo zambiri.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 12:14
6 Mawu Ofanana  

Pakuti monga thupi lili limodzi, nilikhala nazo ziwalo zambiri; koma ziwalo zonse za thupilo, pokhala zambiri, zili thupi limodzi; momwemonso Khristu.


Ngati phazi likati, Popeza sindili dzanja, sindili wa thupi; kodi silili la thupi chifukwa cha ichi?


Koma ngati zonse zikadakhala chiwalo chimodzi, likadakhala kuti thupi?


Koma tsopano pali ziwalo zambiri, koma thupi limodzi.


Mwa ichi, mutataya zonama, lankhulani zoona yense ndi mnzake; pakuti tili ziwalo wina ndi mnzake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa