1 Akorinto 11:32 - Buku Lopatulika32 Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Koma Ambuye amatilanga, kuti tiphunzirepo nzeru, kuwopa kuti tingaimbidwe mlandu pamodzi ndi anthu odalira zapansipano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Pamene tiweruzidwa ndi Ambuye, ndiye kuti akukonza khalidwe lathu kupewa kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi anthu osakhulupirira. Onani mutuwo |