Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 11:31 - Buku Lopatulika

31 Koma ngati tikadadzizindikira tokha sitikadaweruzidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Koma ngati tikadadzizindikira tokha sitikadaweruzidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Tikadadziyang'ana bwino, sitikadalangidwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Koma tikanadziyesa tokha sitikaweruzidwanso.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 11:31
9 Mawu Ofanana  

Koma munthu adziyese yekha, ndi kotero adye mkate, ndi kumwera chikho.


Chifukwa chake ambiri mwa inu afooka, nadwala, ndipo ambiri agona.


Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi.


Ngati tivomereza machimo athu, ali wokhulupirika ndi wolungama Iye, kuti atikhululukire machimo athu, ndi kutisambitsa kutichotsera chosalungama chilichonse.


Potero kumbukira kumene wagwerako, nulape, nuchite ntchito zoyamba; koma ngati sutero, ndidzadza kwa iwe, ndipo ndidzatunsa choikaponyali chako, kuchichotsa pamalo pake, ngati sulapa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa