1 Akorinto 11:30 - Buku Lopatulika30 Chifukwa chake ambiri mwa inu afooka, nadwala, ndipo ambiri agona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Chifukwa chake ambiri mwa inu afooka, nadwala, ndipo ambiri agona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Nchifukwa chake ambiri mwa inu akudwala, akufooka, ndipo ena amwalirapo kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Nʼchifukwa chake pakati panu ambiri mwa inu ndi ofowoka ndi odwala, ndipo ambirinso agona tulo. Onani mutuwo |