Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 11:28 - Buku Lopatulika

28 Koma munthu adziyese yekha, ndi kotero adye mkate, ndi kumwera chikho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Koma munthu adziyese yekha, ndi kotero adye mkate, ndi kumwera chikho.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Koma munthu aziyamba wadziwona bwino asanadyeko mkate umenewu ndi kumwa chikho chimenechi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Munthu adzisanthule yekha asanadye buledi kapena kumwa chikhochi.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 11:28
13 Mawu Ofanana  

Tisanthule ntiyese njira zathu ntibwerenso kwa Yehova.


Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.


Atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.


Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye?


Pakuti iye wakudya ndi wakumwa, adya namwa chiweruziro kwa iye yekha, ngati sazindikira thupilo.


Koma ngati tikadadzizindikira tokha sitikadaweruzidwa.


Dziyeseni nokha, ngati muli m'chikhulupiriro, dzitsimikizeni nokha. Kapena simuzindikira kodi za inu nokha kuti Yesu Khristu ali mwa inu? Mukapanda kukhala osatsimikizidwa.


Koma yense ayesere ntchito yake ya iye yekha, ndipo pamenepo adzakhala nako kudzitamandira chifukwa cha iye yekha, si chifukwa cha wina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa