1 Akorinto 11:26 - Buku Lopatulika26 Pakuti nthawi zonse mukadya mkate uwu ndi kumwera chikho, mulalikira imfa ya Ambuye kufikira akadza Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pakuti nthawi zonse mukadya mkate uwu ndi kumwera chikho, mulalikira imfa ya Ambuye kufikira akadza Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Pakuti nthaŵi zonse mukamadya mkate umenewu, ndi kumwa chikho chimenechi, mumalalika imfa ya Ambuye, mpaka adzabwerenso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Pakuti nthawi zonse pamene mudya bulediyu ndikumwa chikhochi, mukulalikira imfa ya Ambuye mpaka Iye adzabweranso. Onani mutuwo |