1 Akorinto 11:18 - Buku Lopatulika18 Pakutitu poyamba posonkhana inu mu Mpingo, ndimva kuti pakhala malekano mwa inu; ndipo ndivomereza penapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakutitu poyamba posonkhana inu mu Mpingo, ndimva kuti pakhala malekano mwa inu; ndipo ndivomereza penapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Choyamba, ndikumva kuti mukamasonkhana mu mpingo, mumapatulana. Ndipo ndikhulupirira kuti zimenezi kwinaku nzoona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Choyamba, ndikumva kuti mukasonkhana mu mpingo mumasankhana ndipo ndikukhulupirira kuti zimenezi kwinaku nʼzoona. Onani mutuwo |