1 Akorinto 11:17 - Buku Lopatulika17 Koma pakulalikira ichi sinditama inu, popeza simusonkhanira chokoma, koma choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma pakulalikira ichi sinditama inu, popeza simusonkhanira chokoma, koma choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsopano pali mfundo ina imene sindingakuyamikireni. Ndiye kuti misonkhano yanu imabweretsa zoipa osati zabwino ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma popereka malangizo awa sindikufuna kukuyamikirani popeza mʼmisonkhano yanu mumachita zoyipa kuposa zabwino. Onani mutuwo |