1 Akorinto 11:14 - Buku Lopatulika14 Kodi ubadwidwe womwe sutiphunzitsa kuti ngati mwamuna aweta tsitsi chinyozetsa iye? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Kodi ubadwidwe womwe sutiphunzitsa kuti ngati mwamuna aweta tsitsi chinyozetsa iye? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kodi chibadwa chathu chomwe sichitiphunzitsa kuti nchamanyazi kwa mwamuna kukhala ndi tsitsi lalitali, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kodi chikhalidwe chathu sichitiphunzitsa kuti nʼchamanyazi kuti mwamuna akhale ndi tsitsi lalitali, Onani mutuwo |