Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -

Estere INTRO1 - Buku Lopatulika

1

Mau Oyamba
Bukuli likukamba za Estere, mtsikana wina wachiyuda, amene ankakonda kwambiri anthu a mtundu wake, naonetsa kulimba mtima kwake pothandiza kuwapulumutsa Ayudawo kwa adani ao. Lifotokozanso za chiyambi chake komanso tanthauzo la chikondwerero cha Chiyuda chotchedwa Purimu.
Za mkatimu
Estere asankhidwa kuti akhale mfumukazi kudziko la Persiya 1.1—2.23
Hamani apanga chiwembu chofuna kuwonongeratu fuko la Ayuda 3.1—5.14
Hamani atsutsidwa naphedwa 6.1—7.10
Ayuda agonjetsa adani ao 8.1—10.3

Bible Society of Malawi

Bible Society of Malawi
Titsatireni:



Zotsatsa