Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -

2 Yohane INTRO1 - Buku Lopatulika

1

Mau Oyamba
Kalata yachiwiri yolembedwa ndi mtumwi Yohane inalembedwa ndi “Mkuluyo” kupita kwa “mkazi womveka wosankhika, ndi ana ake”, amene mwina akutanthauza mpingo ndi anthu ake. Uthenga wake ndi waufupi ndipo ndi wolimbitsana za kukondana komanso kuchenjeza za aphunzitsi onyenga ndi ziphunzitso zawo zachinyengo.
Za mkatimu
Mau oyamba 1.1-3
Kufunikira kwa chikondi 1.4-6
Awachenjeze asatsate ziphunzitso zonyenga 1.7-11
Mau omaliza 1.12-13

Bible Society of Malawi

Bible Society of Malawi
Titsatireni:



Zotsatsa