Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 8:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo



Numeri 8:1
6 Mawu Ofanana  

Ana aamuna a Levi ndi awa: Geresoni, Kohati ndi Merari.


“Upange choyikapo nyale chagolide wabwino kwambiri. Tsinde lake ndi mphanda zake zikhale zosulidwa ndi nyundo. Zikho zake zokhala ndi mphukira ndi maluwa ake zipangidwire kumodzi.


Koma mabanja a fuko la Levi okha sanawawerenge pamodzi ndi ena.


Mose atalowa mu tenti ya msonkhano kukayankhula ndi Yehova, anamva mawu kuchokera pakati pa Akerubi awiri amene anali pamwamba pa chivundikiro cha bokosi la umboni. Ndipo anayankhula naye.


“Yankhula ndi Aaroni kuti pamene uyimika nyale zisanu ndi ziwiri, nyalezo ziziyaka kutsogolo kwa choyikapo nyale.”


Pa nthawi imeneyo Yehova anapatula fuko la Levi kuti anyamule bokosi la pangano la Yehova lija, kuti ayimirire pamaso pa Yehova, kutumikira ndi kunena madalitso pa dzina lake monga amachitira mpaka lero.