Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 5:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aisraeli anachitadi zimenezi. Anawatulutsira kunja kwa msasa monga momwe Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo ana a Israele anachita chotero, nawatulutsira kunja kwa chigono; monga Yehova adanena ndi Mose momwemo ana a Israele anachita.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Israele anachita chotero, nawatulutsira kunja kwa chigono; monga Yehova adanena ndi Mose momwemo ana a Israele anachita.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Aisraele adachitadi zimenezi, ndipo adaŵatulutsira kunja anthuwo. Ankachitadi monga momwe Chauta adaauzira Mose.

Onani mutuwo



Numeri 5:4
5 Mawu Ofanana  

Mfumu Uziya anali ndi khate mpaka tsiku limene anamwalira. Iye amakhala mʼnyumba ya yekha ngati wakhate, ndipo samalowa mʼNyumba ya Yehova. Yotamu mwana wake ndiye amayangʼanira nyumba yaufumu ndipo ankalamulira anthu a mʼdzikomo.


Aisraeli anachita monga momwe Yehova analamulira Mose ndi Aaroni.


“Aisraeli onse anachita monga momwe Yehova analamulira Mose ndi Aaroni.


Muchotse amuna komanso amayi ndipo muwatulutsire kunja kwa msasa kuti asadetse msasa wawo kumene Ine ndimakhala pakati pawo.”


Yehova anati kwa Mose,