Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Utatha mliri Yehova anati kwa Mose ndi Eliezara mwana wa Aaroni,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Utatha mliriwo, Chauta adauza Mose ndi Eleazara, mwana wa wansembe Aroni, kuti,

Onani mutuwo



Numeri 26:1
3 Mawu Ofanana  

monga momwe Yehova analamulira Mose. Motero iyeyo anawawerenga mʼchipululu cha Sinai:


chifukwa ankakuonani inu ngati adani awo pamene anakupusitsani pa nkhani ya ku Peori, ndiponso za mlongo wawo Kozibi, mwana wamkazi wa mtsogoleri wa Amidiyani, mkazi yemwe anaphedwa pamene mliri unabwera chifukwa cha zimene zinachitika ku Peori.”


Pa mliriwo, anthu okwana 24,000 anafa.