Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 57,400.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo ankhondo ake ngokwanira 57,400.

Onani mutuwo



Numeri 2:8
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Zebuloni chinali 57,400.


Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.


Anthu onse aamuna mʼmisasa ya Yuda, chiwerengero chawo ndi 186,400 monga mwa magulu awo. Iwowo ndiwo aziyamba kusamuka.