Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono pabwere fuko la Zebuloni, limene mtsogoleri wake ndi Eliyabu mwana wa Heloni,

Onani mutuwo



Numeri 2:7
7 Mawu Ofanana  

Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,


Eliabu mwana wa Heloni ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Zebuloni.


Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 54,400.


Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 57,400.


Pa tsiku lachitatu, Eliabu mwana wa Heloni, mtsogoleri wa Azebuloni, anabweretsa chopereka chake.


ndi ngʼombe ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Eliabu mwana wa Heloni.