Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Fuko la Isakara lidzamanga pafupi ndi Yuda. Mtsogoleri wa gulu la Isakara ndi Netanieli mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Isakara; ndipo kalonga wa ana a Isakara ndiye Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Isakara; ndipo kalonga wa ana a Isakara ndiye Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amene amange pafupi ndi fuko lake akhale a fuko la Isakara. Mtsogoleri wa fuko la Isakaralo ndi Netanele mwana wa Zuwara,

Onani mutuwo



Numeri 2:5
8 Mawu Ofanana  

Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,


Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanieli mwana wa Zuwara,


Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 74,600.


Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 54,400.


Pa tsiku lachiwiri, Natanieli mwana wa Zuwara, mtsogoleri wa Isakara, anabweretsa chopereka chake.


ndi ngʼombe ziwiri, nkhosa zazimuna ziwiri, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa asanu a chaka chimodzi, nsembe ya chiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Netanieli mwana wa Zuwara.