Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Motero malowo anawatcha Tabera, chifukwa moto wa Yehova unayaka pakati pawo.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo anatcha malowo dzina lake Tabera; popeza moto wa Yehova udayaka pakati pao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatcha malowo dzina lake Tabera; popeza moto wa Yehova udayaka pakati pao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero malowo adaŵatcha Tabera, chifukwa choti moto wa Chauta udayaka pakati pao.

Onani mutuwo



Numeri 11:3
4 Mawu Ofanana  

Yehova atawamva anakwiya kwambiri; moto wake unayaka kutsutsana ndi Yakobo, ndipo mkwiyo wake unauka kutsutsana ndi Israeli,


Anthu ena osokoneza amene anali pakati pa Aisraeli anayamba kukhumba chakudya cha ku Igupto ndipo Aisraeli nawonso anayamba kufuwula kwambiri nʼkumati, “Tikanangopeza nyama yoti nʼkudya!


Ndipo moto wochokera kwa Yehova unabwera nʼkunyeketsa anthu 250 amene ankapereka nsembe yofukiza aja.


Inu munamukwiyitsanso Yehova ku Tabera, ku Masa ndi ku Kibiroti Hatava.