Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene akuliza malipenga onse awiri, anthu onse asonkhane kwa iwe pa khomo la tenti ya msonkhano.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Akaliza, khamu lonse lisonkhane kuli iwe ku khomo la chihema chokomanako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akaliza, khamu lonse lisonkhane kuli iwe ku khomo la chihema chokomanako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akaliza aŵiri onsewo, mpingo wonse usonkhane kwa iwe pa chipata cha chihema chamsonkhano.

Onani mutuwo



Numeri 10:3
3 Mawu Ofanana  

“Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti, ‘Lizani lipenga mʼdziko lonse!’ Ndipo fuwulani kuti, ‘Sonkhanani! Tiyeni tithawire ku mizinda yotetezedwa!’


Lizani lipenga mu Ziyoni. Chenjezani pa phiri langa loyera. Onse okhala mʼdziko anjenjemere, pakuti tsiku la Yehova likubwera, layandikira;