Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo



Numeri 1:9
5 Mawu Ofanana  

Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri;


Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,


Eliabu mwana wa Heloni ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Zebuloni.


Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.


Pa tsiku lachitatu, Eliabu mwana wa Heloni, mtsogoleri wa Azebuloni, anabweretsa chopereka chake.