Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Isakara, Netanele mwana wa Zuwara;

Onani mutuwo



Numeri 1:8
5 Mawu Ofanana  

Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,


Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,


Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanieli mwana wa Zuwara,


Fuko la Isakara lidzamanga pafupi ndi Yuda. Mtsogoleri wa gulu la Isakara ndi Netanieli mwana wa Zuwara.


Pa tsiku lachiwiri, Natanieli mwana wa Zuwara, mtsogoleri wa Isakara, anabweretsa chopereka chake.