Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu;

Onani mutuwo



Numeri 1:7
11 Mawu Ofanana  

Aaroni anakwatira Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wa Nasoni ndipo Iye anabereka Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.


Selumieli mwana wa Zurisadai, kuchokera ku fuko la Simeoni,


Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,


Magulu a msasa wa Yuda ndiwo anayamba kunyamuka potsata mbendera yawo. Mtsogoleri wa gulu lawo anali Naasoni mwana wa Aminadabu.


Kummawa, kotulukira dzuwa, magulu a msasa wa Yuda amange pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Ayudawo ndi Naasoni mwana wa Aminadabu.


Amene anabweretsa chopereka chake tsiku loyamba anali Naasoni mwana wa Aminadabu wa fuko la Yuda.


mwana wa Yese, mwana wa Obedi, mwana wa Bowazi, mwana wa Salimoni, mwana wa Naasoni,


Izi tsono ndizo zidzukulu za Perezi: Perezi anali abambo a Hezironi.


Aminadabu abambo a Naasoni, Naasoni anali abambo a Salimoni,