Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Selumieli mwana wa Zurisadai, kuchokera ku fuko la Simeoni,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai;

Onani mutuwo



Numeri 1:6
5 Mawu Ofanana  

Mayina a anthu amene akuthandizeniwo ndi awa: Elizuri mwana wa Sedeuri, kuchokera ku fuko la Rubeni,


Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,


Mtsogoleri wa fuko la Simeoni anali Selumieli mwana wa Zurisadai,


Fuko la Simeoni lidzamanga pafupi ndi Rubeni. Mtsogoleri wa gulu la Simeoni ndi Selumieli mwana wa Zurisadai.


Pa tsiku lachisanu Selumieli mwana wa Zurisadai, mtsogoleri wa fuko la Simeoni, anabweretsa chopereka chake.