Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 127:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ana a ubwana wake wa munthu akunga mivi m'dzanja lake la chiphona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana a ubwana wake wa munthu akunga mivi m'dzanja lake la chiphona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana apaunyamata ali ngati mivi m'manja mwa munthu wankhondo.

Onani mutuwo



Masalimo 127:4
4 Mawu Ofanana  

Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.


Zidzukulu ndiye ulemu wa anthu okalamba, ndipo makolo ndiye ulemerero wa ana.


Ana ake amamunyadira ndipo amamutcha kuti wodala; ndipo mwamuna wake, amamuyamikira nʼkumati,


Taonani, ndidzaukitsa gulu lankhondo lamphamvu la mitundu ina ndi kubwera nalo kuchokera kumpoto kudzamenyana ndi Babuloni. Iwo adzandandalika ankhondo awo ndi kugonjetsa Babuloni. Mivi yawo ili ngati ya ankhondo aluso, yosapita padera.