Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 8:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ngati simulola kuti apite Ine ndidzalanga dziko lonse la Igupto polidzaza ndi achule.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo ukakana kuwalola amuke, taona, Ine ndidzapanda dziko lako lonse ndi achule;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ukakana kuwalola amuke, taona, Ine ndidzapanda dziko lako lonse ndi achule;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ukakana kuŵalola, dziko lako lonse ndidzalilanga polidzaza ndi achule.

Onani mutuwo



Eksodo 8:2
7 Mawu Ofanana  

Dziko lawo linadzaza ndi achule amene analowa mʼzipinda zogona za olamulira awo.


Iye anawatumizira magulu a ntchentche zimene zinawawononga, ndiponso achule amene anawasakaza.


Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Farao ndi wowuma mtima. Akukana kulola anthu anga kuti apite.


Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Ukamuwuze Farao kuti, Lolani anthu anga kuti apite, akandipembedze.


Mtsinje wa Nailo udzadzaza ndi achule. Achulewo adzatuluka ndi kukalowa mʼnyumba yaufumu, ku chipinda chogona ndi pa bedi lako, mʼnyumba za nduna zako ndi pa anthu ako ndi mophikira buledi ndiponso mopangira bulediyo.


Koma ngati ukana kuti apite ndi kupitiriza kuwaletsa,