Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 7:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni,

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo



Eksodo 7:8
3 Mawu Ofanana  

Mose anali ndi zaka 80, ndipo Aaroni anali ndi zaka 83 pamene anakayankhula kwa Farao.


“Ngati Farao adzati kwa inu, ‘Chitani chozizwitsa,’ iwe Mose udzati kwa Aaroni, ‘Tenga ndodo yako ndipo uyiponye pamaso pa Farao,’ ndipo idzasanduka njoka.”


zizindikiro zozizwitsa zimene anazionetsa ndi zinthu zimene anazichita mʼkati mwa Igupto, Farao mfumu ya Igupto ndi kwa dziko lake lonse;