Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 2:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atayangʼana uku ndi uku, naona kuti panalibe wina aliyense, Mose anamupha Mwiguptoyo ndipo anamukwirira mu mchenga.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo anaunguza kwina ndi kwina, ndipo pamene anaona kuti palibe munthu, anakantha Mwejipito, namfotsera mumchenga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anaunguza kwina ndi kwina, ndipo pamene anaona kuti palibe munthu, anakantha Mwejipito, namfotsera mumchenga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Mose atayang'ana uku ndi uku, naona kuti kulibe anthu, adamupha Mwejipitoyo, nafotsera mtembo wake mu mchenga.

Onani mutuwo



Eksodo 2:12
1 Mawu Ofanana