Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 2:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo munthu wina wa fuko la Levi anakwatira mkazi wa fuko lomwelo.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu wina wa fuko la Levi adakwatira mkazi wa fuko lomwelo.

Onani mutuwo



Eksodo 2:1
6 Mawu Ofanana  

Israeli akanali mʼderali, Rubeni anapita nakagonana ndi Biliha, mdzakazi wa abambo ake. Yakobo uja anazimva zimenezi. Yakobo anali ndi ana aamuna khumi ndi awiri:


Koma Hadadi akanali mwana anathawira ku Igupto pamodzi ndi akuluakulu ena a ku Edomu amene ankatumikira abambo ake.


Dzina la mkazi wa Amramu linali Yokobedi, mdzukulu wa Levi, yemwe anabadwa mwa Alevi mu Igupto. Yokobedi anaberekera Amramu Aaroni, Mose ndi Miriamu mlongo wawo.