Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 13:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku la lero mwezi uno wa Abibu, mukutuluka mʼdziko la Igupto.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mukuchoka ku Ejipito pa tsiku lalero, mwezi uno wa Abibu.

Onani mutuwo



Eksodo 13:4
6 Mawu Ofanana  

Patapita mibado inayi, adzukulu ako adzabwereranso kuno popeza tchimo la Aamori silinafike pachimake kuti alangidwe.”


“Mwezi uno uzikhala mwezi wanu woyamba wa chaka.


“Muzichita Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti. Kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti monga ndinakulamulirani. Muzichita zimenezi mwezi wa Abibu pa nthawi yomwe ndayika, pakuti mʼmwezi umenewu munatuluka mʼdziko la Igupto. “Pasapezeke munthu wobwera pamaso panga wopanda kanthu mʼmanja.


“Muzichita chikondwerero cha buledi wopanda yisiti. Kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti monga momwe ndinakulamulirani. Muzichita zimenezi pa nthawi yoyikika mwezi wa Abibu, pakuti mwezi umenewu inu munatuluka mʼdziko la Igupto.


Ndinakhazikitsa pangano langa ndi iwo kuwalonjeza kuti ndidzawapatsa dziko la Kanaani kumene anakhalako kale ngati alendo.