Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 7:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mʼnyangayo munatuluka zirombo zazikulu zinayi, chilichonse chosiyana ndi chinzake.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo zinatuluka m'nyanja zilombo zazikulu zinai zosiyanasiyana.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo zinatuluka m'nyanja zilombo zazikulu zinai zosiyanasiyana.

Onani mutuwo



Danieli 7:3
9 Mawu Ofanana  

Wolemekezeka ndinu, wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.


‘Zirombo zikuluzikulu zinayi zija ndi maufumu anayi amene adzaoneka pa dziko lapansi.


Ndipo ndinaona chirombo chikutuluka mʼnyanja. Chinali ndi nyanga khumi ndi mitu isanu ndi iwiri. Pa nyanga iliyonse chinavala chipewa chaufumu, ndipo pa mutu uliwonse panali dzina lonyoza Mulungu.


Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera.