Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 11:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo chaka choyamba cha Dariyo Mmedi ine Mikayeli ndinabwera kumuthandiza ndi kumuteteza Gabrieli.

Onani mutuwo

Buku Lopatulika

Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa.

Onani mutuwo



Danieli 11:1
6 Mawu Ofanana  

Tamandani Yehova, inu angelo ake, amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula, amene mumamvera mawu ake.


Kenaka wooneka ngati munthu uja anandikhudzanso ndipo anandipatsa mphamvu.


ndipo Dariyo Mmedi analanda ufumuwo ali ndi zaka 62.


Kunamukomera Dariyo kusankha akalonga 120 kuti alamulire mu ufumu wonse,


Mʼchaka choyamba cha Dariyo mwana wa Ahasiwero (wochokera kwa Amedi), amene anakhala mfumu ya ku Babuloni,


Kumeneko analimbikitsa mitima ya ophunzira ndi kuwapatsa mphamvu kuti akhalebe woona mʼchikhulupiriro. Iwo anati, “Ife tiyenera kudutsa mʼmasautso ambiri kuti tikalowe mu ufumu wa Mulungu.”